Categories
YUDA

YUDA Mau Oyamba

Mau Oyamba

Kalata yolembedwa ndi mtumwi Yuda

analembedwa pofuna kuwachenjeza za aphunzitsi onyenga amene amadzitcha okhulupirira. M’kalata iyi yachidule imene nkhani zake zikufanana ndi za mu

Kalata yachiwiri yolembedwa ndi mtumwi Petro

, ndipo wolembayo akuwalimbikitsa awerengi ake kuti “mulimbanetu chifukwa cha chikhulupiriro chapatsidwa kamodzi kwa oyera mtima”.

Za mkatimu

Mau oyamba 1.1-2

Khalidwe labwino, chiphunzitso, ndi mathero a aphunzitsi onyenga 1.3-16

Awalimbikitsa asunge chikhulupiriro 1.17-23

Mdalitso 1.24-25

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *