Mau Oyamba
Bukuli likamba za mfumu Solomoni ndi mafumu a ku Yuda okha mpaka nthawi ya kupasuka kwa mzinda wa Yerusalemu.
Za mkatimu
Ufumu wa Solomoni
1.1—9.31
a. Zaka zoyamba za ufumu wake
1.1-17
b. Amanga Kachisi wa Yehova
2.1—7.10
c. Zaka zotsiriza za ufumu wake
7.11—9.31
Za mafumu ena a ku Yuda
10.1—36.23
a. Mafumu akumpoto aukira ufumu wa Rehobowamu
10.1-19
b. Mafumu a ku Yuda
11.1—36.12
c. Kupasuka kwa mzinda wa Yerusalemu
36.13-23