Afulumizidwa anthu kulemekeza Yehova
Nyimbo yokwerera.
1 Taonani, lemekezani Yehova, atumiki a Yehova inu nonse,
akuimirira m’nyumba ya Yehova usiku.
2 Kwezani manja anu kumalo oyera,
nimulemekeze Yehova.
3 Yehova, ali muZiyoni, akudalitseni;
ndiye amene analenga kumwamba ndi dziko lapansi.
—https://api-cdn.youversionapi.com/audio-bible-youversionapi/355/32k/PSA/134-c0ab6cf3799896400acd612283803b61.mp3?version_id=1068—