Categories
NAHUMU

NAHUMU Mau Oyamba

Mau Oyamba

Bukuli ndi ndakatulo yokondwerera kupasuka kwa Ninive, mzinda waukulu wa Aasiriya amene ankazunza Aisraele kuyambira kale. Kupasuka kwa mzindawo kuwoneka ngati chilango cha Mulungu chogwera anthu onyada ndi ankhanza.

Za mkatimu

Chauta aimba Ninive mlandu

1.1-15

Kupasuka kwa mzindawo

2.1—3.19

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *