Categories
MASALIMO

MASALIMO 134

Afulumizidwa anthu kulemekeza Yehova

Nyimbo yokwerera.

1 Taonani, lemekezani Yehova, atumiki a Yehova inu nonse,

akuimirira m’nyumba ya Yehova usiku.

2 Kwezani manja anu kumalo oyera,

nimulemekeze Yehova.

3 Yehova, ali muZiyoni, akudalitseni;

ndiye amene analenga kumwamba ndi dziko lapansi.

—https://api-cdn.youversionapi.com/audio-bible-youversionapi/355/32k/PSA/134-c0ab6cf3799896400acd612283803b61.mp3?version_id=1068—

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *