Mau Oyamba
Kalata yachitatu yolembedwa ndi mtumwi Yohane
inalembedwa ndi “Mkuluyo” kulembera mtsogoleri wa mpingo dzina lake Gayo. Mlembiyo akumuyamikira Gayo chifukwa cha kuthandiza Akhristu ena, komanso akuwachenjeza za munthu wina dzina lake Diotrefe.
Za mkatimu
Mau oyamba 1.1-4
Gayo akumulemekeza 1.5-8
Diotrefe akumudzudzula 9-10
Demetrio akumuyamikira 1.11-12
Mau omaliza 1.13-15