Categories
2 MBIRI

2 MBIRI Mau Oyamba

Mau Oyamba

Bukuli likamba za mfumu Solomoni ndi mafumu a ku Yuda okha mpaka nthawi ya kupasuka kwa mzinda wa Yerusalemu.

Za mkatimu

Ufumu wa Solomoni

1.1—9.31

a. Zaka zoyamba za ufumu wake

1.1-17

b. Amanga Kachisi wa Yehova

2.1—7.10

c. Zaka zotsiriza za ufumu wake

7.11—9.31

Za mafumu ena a ku Yuda

10.1—36.23

a. Mafumu akumpoto aukira ufumu wa Rehobowamu

10.1-19

b. Mafumu a ku Yuda

11.1—36.12

c. Kupasuka kwa mzinda wa Yerusalemu

36.13-23

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *